Skip to main content
Spotify for Podcasters
Chiphunzitso Choona | Sound Doctrine from Gospel Life

Chiphunzitso Choona | Sound Doctrine from Gospel Life

By Gospel Life

Sermons and teaching in Chichewa and English from the ministry of Gospel Life Baptist Mission.
Available on
Apple Podcasts Logo
Google Podcasts Logo
Overcast Logo
Pocket Casts Logo
RadioPublic Logo
Spotify Logo
Currently playing episode

Mulungu ndi wamkulu kuposa mitima yathu/God is greater than our hearts

Chiphunzitso Choona | Sound Doctrine from Gospel LifeFeb 27, 2023

00:00
40:07
Mulungu ndi wamkulu kuposa mitima yathu/God is greater than our hearts

Mulungu ndi wamkulu kuposa mitima yathu/God is greater than our hearts

1 Yohane 3:19-24, kulimbika mtima pamaso pa mulungu kumathandiza ife kuzindikira kuti tili pa choonadi ndipo timakhala okhazikika mtima pa maso pa mulungu. Ife timalandira chilichonse tipempha kwa iye, chifukwa timamvera malamulo ake ndi kuchita zimene zimamukondweretsa. Nthawi imene tichita izi; iye amakhala mwa ife ndipo ife timakhala mwa iye. 1 John 3:19-24, as we are strong hearted and stead fast before God, we are helped to realise that we stand in truth and we are at peace within our hearts before God. we receive all that we ask from God, because we listen to him and his commands and do all that he asks of us. All the time as we do this, he lives in us and we live in him. 
Feb 27, 202340:07
Chikondi pa wina ndi mnzake ndi m'choonadi/Love for one another and in truth

Chikondi pa wina ndi mnzake ndi m'choonadi/Love for one another and in truth

1 Yohane 3:11-18, mawu awa akutikumbutsa za chikondi chathu pa wina ndi mnzake makamaka pamene ife tsono ndi ake a mulungu, chikondi chathu chisakhale cha pakamwa koma cha ntchito zathu ndi m'choonadi kuwonetsera chiyanjano chathu ndi mulungu wathu mwa ambuye wathu Yesu Khristu. 1 John 3:11-18, these words are reminding us of our love for one another especially now that we are children of God, our love for each other should not be in words only but in works also and in truth showing our fellowship with God through our lord Jesus Christ.  
Feb 21, 202301:08:35
Ana A Mulungu/The Children Of God

Ana A Mulungu/The Children Of God

1 Yohane 2:28-3:1-10, mawu a mulungu awa akuthandiza onse omwe ndi ake mulungu kuzindikira kuti pamene ife tagulidwa ndi mwazi wake wa Yesu khristu ndife tsopano ana a mulungu. Ana a mulungu amachita chilungamo ndipo ndiwolungama. Onse omwe alimwa khristu amafanana naye iye. Koma ngati pakati pathu pali ena omwe sachita chilungamo ngakhalenso sakonda m'bale wawo, amenewo siake a mulungu koma a mdierekezi. 1 John 2:28-3:1-10, these words of God are helping us all, children of God to realise that when we were bought by the blood of Christ Jesus, we became his. And now we are known as children of God. The children of God are evident by this fact that whoever does practice righteousness and is just belongs to God. But if one does not, even to love his brother becomes a problem for him then he is of the Devil.   
Feb 15, 202347:02
Khalani mwa Khristu/Remain in Christ

Khalani mwa Khristu/Remain in Christ

1 Yohane 2:18-27, nthawi zambiri anthu amafunsa kuti kodi 'tili nthawi ya masiku omaliza?' Yankho ndi eya. Nthawi ya masiku omaliza ndi pakati pa kubwera kwa Yesu Khristu koyamba ndi kubwera kwa Yesu Khristu kachiwiri. Bukuli likubweretsa poyera nkhani imene ndiyovuta kuyimvetsa. Kodi okana Khristu abwera liti? Paulo akunena motere pakhaniyi, okana Khristu wamkulu adzabwera koma chidwichathu chikhale apa, okana khristu ambiri afika kale. Ndipo ambiri alipakati pathu, mipingo mwadzadza ndi anthu oterewa. Funso nati, kodi ife tili mwa Khristu, kapena gawo lathu ndi lokana Khristu? 1 John 2:18-27, many times people ask in wonder, are we in the ladder days? The answer is yes. The time between the first coming of Jesus Christ an his second coming marks the end of times or the ladder days. This book brings to light about the most confusing story about the anti christ. About the anti christ, When is the anti christ coming? Paul tells us clear that the great anti christ is coming but our focus should be at the anti christ who are already here. many of them are among us, and in our midst they are rejecting christ. But the question still remains, are we remaining in christ or are we partaking the anti christ?   
Feb 10, 202338:34
Kondani Mulungu/Love God

Kondani Mulungu/Love God

1 Yohane 2:12-17,chifukwa chachikondi chimene tilinacho pa mulungu wathu, timamumvera ndi kutsatira malamulo ake. Choncho timawonetsera ku dziko lonse kuti ndife ake kudzera muchikondi chomwe tilinacho pa mulungu wathu. Ndichifukwa chake abale tiyeni tipitirize monga okhulupirira komanso okonda mulungu ndi kukana dziko lapansi. 1 John 2:12-17, because of the love we have for God, we continue to love him more. Through our faith, we continue to also obey his commandments. We continue to show the world that we belong to God and that we love him through our living as christians. It is also the reason why brothers, we should continue to love God and continue living as christians and denying the offers of the world.
Feb 07, 202356:35
Kumvera Mulungu ndi Malamulo ake/Obedient to God and his commandment

Kumvera Mulungu ndi Malamulo ake/Obedient to God and his commandment

1 Yohane 2:3-11, Buku la 1 Yohane likupitiriza kubwera poyera njira zomwe khristu opulumutsidwa akuyenera kupitiriza kuyenda pa nthawi imene khristu wapulumutsidwa. Kumvera mulungu ndi malamulo ake ndi chiwonetsero chachikulu ndi chilungamo chathu kwa anthu kuti ife timankonda mulungu, timakhulupirira mulungu wathu, zonse zimene mulungu atilamulira kuti tichite ife timamvera ndikuchita. 1 John 2:3-11, the book of 1 John continues to shade light on principles that true christians are continuously to show in the congregation and to the people who are not part of the church and are regarded as non believers. Obedient to God and his principles shows a sign and our justice to others that we love God and that we obey his principles and all that God commands us we willingly do.       
Jan 25, 202358:10
Kuyenda mu kuwunika(khalidwe loyamba)/Walking in the light(the first attribute)

Kuyenda mu kuwunika(khalidwe loyamba)/Walking in the light(the first attribute)

1 Yohane 1:5-2:2, kutchulidwa kuti nkhristu sikungapangise munthu kukhala ndi zimene nkhristu ali nazo. Bukuli muli njira zomwe akhristu akuyenera kuyenda pa chikhristu chawo. Chiyambi cha bukuli tikupeza chiphunzitso cha moyo. Akhristu amene alandira moyo ndipo ali ndi moyo tsopano akuyenera kuyenda mu kuwunika chifukwa ali pa chiyanjano ndi mulungu amene ndi kuwunika. 1 John 1:5-2:2, to be called a christian cannot make one get all the things a christian has. In this book, many ways are listed for christians to follow when walking in their christianity. The beginning of this book, we read about life. Christians who have received life and now they have life are suppose to walk in the light because they have  fellowship with God who is light.  
Jan 22, 202358:44
Makhalidwe a chiyanjano mu mpingo/attributes of fellowship in the church

Makhalidwe a chiyanjano mu mpingo/attributes of fellowship in the church

1 Yohane 1:1-4, moyo weniweni umachokera kwa mulungu ndipo ndi moyo wosatha. Kodi ife tili ndi moyo wosatha? Mulungu amapereka moyo wosatha, ndiye  Yesu Khristu. Uthenga wabwino umabweretsa chiyanjano pakati pa akhristu mu mpingo. Ngati tili ndi moyo wosatha, tidzakhala pa chiyanjano ndi atate ndi mwana ndi mzimu woyera ndi wina ndi zake. Tikuyenera kukhala ndi chiyanjano chimene ndi moyo wosatha. 1 John 1:1-4, the real life we spoke about, really comes from God and its everlasting life. But do we have everlasting life? God gives his sheep everlasting life and that everlasting life is Jesus Christ. The good news brings about fellowship among christians in the church. If christians have everlasting life, it is evident that they have fellowship with the father, the son, and the Holy Spirit and with their fellow christians. 
Jan 18, 202301:00:11
Za mkati mwa buku la 1 Yohane/Inside the book of 1 John

Za mkati mwa buku la 1 Yohane/Inside the book of 1 John

1 Yohane, buku limeneli likupezeka ndi uthenga opasa moyo. Nkhani zomwe zikupezeka mu bukuli kwambiri ndi ndondomeko za kayendedwe ka khristu kuti ndi ziti zomwe akuyenera kuchita khristu komanso ndi ziti zomwe sakuyenera kuchita pamene iye wa pulumutsidwa kapena pamene iye watchulidwa kuti ndi khristu. Khristu aliyense amakhala khristu pamene wabatizidwa ndipo pamene mzimu woyera ali mwa iye. Ndondomeko yomwe ili mu bukuli ikuthandizira akhristu kuzindikira kuti tsopano ndife akhristu pamene mzimu woyera ali mwa ife.  1 John, this book contains the word of life. This book is mainly about the way of life of christians. It comprises of what christians are suppose to do and are not suppose to do when are saved and have now received the Holy Spirit and are announced as christians. Every person becomes a christian when have been baptised and have received the Holy Spirit because nobody is born that way. So this book it's all about how can a christian recognise the power of the Holy Spirit operating in him or her and one is able to bare good fruits.
Jan 06, 202301:04:39
Mtima ngati wa Khristu Yesu/A heart like that of Christ Jesus

Mtima ngati wa Khristu Yesu/A heart like that of Christ Jesus

Aphilipi 2:5-8, ma vesi amenewa akulimbikitsa akhristu onse kukhala odzichepetsa monga Yesu Khristu anali odzichepetsa. Yesu anavomera kusiya ulemerero wake ku dziko la kumwamba ndi kubadwira ku banja losauka, kubadwira anthu osauka ndi cholinga choti apeleke chipulumutso ku dziko lonse lapansi ndi kupulumutsa anthu onse ochimwa. Chifukwa cha kudzichepetsa kwa Khristu Yesu lero anthu tonse tili ndi kuthekera kokhala moyo wa chiyembekezo ndikulindilira moyo wosatha. Choncho kubadwa kwa Yesu Khristu kukuyenera kusintha machitidwe athu ndi anthu ena. Yesu akulimbikitsa ubale wolimba pakati pa akhristu omwe ndi mboni za iye. Philippians 2:5-8, these verses are encouraging christians to be humble like Jesus Christ was humble. Jesus was humble that he left his glorious home and was born to a poor family and born for poor people so that through that he gives a propitiatory sacrifice for all sinful people and become the salvation for all people. Because of his humbleness, today we have life and hope for the everlasting life to come. In that way, the birth of Jesus Christ should cause christians to have the right attitude towards others. Jesus is encouraging strong brotherhood among fellow christians as we are being his witnesses.
Dec 27, 202257:07
Chisangalaro choonadi pa kubadwa kwa Yesu Khristu/The real happiness upon the birth of Jesus Christ

Chisangalaro choonadi pa kubadwa kwa Yesu Khristu/The real happiness upon the birth of Jesus Christ

Mateyu 2:1-15, kubadwa kwa ambuye Yesu m'mitima mwathu ndi chinthu chonyaditsa kwambiri. Ndipo chisangalaro chake ndichamtengo wapatali. Anzeru akum'mawa anakondwera kwambiri poona mfumu yobadwayo. Kodi nankha ife lero tikamulandira Yesu Khristu ndikukhala ambuye ndi mpulumutsi wathu timakondwerera motani? Matthew 2:1-15, The birth of our lord Jesus in our hearts its a priceless gift. And the happiness that comes with it is also priceless. Wise men from the east upon seeing the king, Jesus Christ they did obeisance to him. And they were really happy after seeing him. What about us today, when we receive christ and acknowledge him as our lord and saviour, how do we celebrate?
Dec 20, 202253:26
Yesu Khristu ndi uthenga wabwino/Jesus Christ is the good news

Yesu Khristu ndi uthenga wabwino/Jesus Christ is the good news

Luka 2:1-14, kubadwa kwa yesu Khristu kunabweretsa chimwemwe pakati pa anthu makamaka okhawo omwe anamudwiwa iye. Ndipo chimwemwe chotere chimapitirira kupezeka pakati pathu. Makamaka mwa ife tonse okhulupirira ndi opulumutsidwa chifukwa timadziwa bwino lomwe kuti Yesu Khristu ndi chifukwa chokhacho tili ndi moyo komanso ndi chiyembekezo. Luke 2:1-14, the birth of Jesus Christ brought happiness amongst those who knew him. And that happiness still lives in us believers today. We well know that Jesus is our lord and saviour. And it's because of him that we now have hope.
Dec 17, 202248:31
Kuyenda m'chikondi/Walking in the love

Kuyenda m'chikondi/Walking in the love

Aefeso 4:1-6, Paulo mtumwi akulimbikitsa a khristu kukhala ndi makhalidwe oyenera mayitanidwe awo. Akhale odzichepetsa kwathunthu ndi ofatsa, oleza  mtima, ololerana wina ndi mzake. Akhristuwa achite zonsezi moyetsetsa kusunga umodzi wa mzimu umene umatimangilira pamodzi ndi mtendere. Ephesians 4:1-6, the apostle Paul is appealing to the christians to walk worthily of the calling with which they were called. With all humility and mildness with patience, putting up with one another in love. Earnestly endeavouring to maintain the oneness of the spirit in the uniting bond of peace.
Nov 28, 202201:07:01
Mpingo ndi thupi la Khristu Yesu/A church is the body of Christ Jesus

Mpingo ndi thupi la Khristu Yesu/A church is the body of Christ Jesus

Afilipi 2:1-4, mundime yamalemba imeneyi Paulo akuthokoza, akulangiza, akulimbikitsa ndi kudzuzura mpingo omwe iye anawuyambitsa ponena kuti "monga mpingo ndi thupi la Khristu Yesu, ziwalo zake kukhala akhristu sakuyenera kukhala ndi migawano, popeza sitingathe kugawa thupi la Khristu Yesu." Motero akulimbikitsa akhristu kukhala ozichepetsa mu mpingo. Philippians 2:1-4, in this passage Paul is extending his gratitude, encouragement, advice and his rebuke to the church he started by saying "as the church is the body of Christ Jesus, its members being the Christians are not suppose to have divisions in the church, just as we cannot divide the body of Christ Jesus." So he is encouraging christians to have humility in the church.
Nov 23, 202201:11:60
Milodzo yolodzera chipulumutso/Signs leading to salvation

Milodzo yolodzera chipulumutso/Signs leading to salvation

Genesis 11:10-32, mibado yonse kuyambira pa Adamu, Seti, Nowa, Semu komanso abramu yemwe anasinthidwa kukhala Abrahamu ikutitengera kwa Yesu Khristu yemwe ndi chipulumutso cha anthu onse. Ife tonse ndiodala kamba koti tilimunthawi yomwe milodzo inafika kumathero ndipo chipulumutso chinapelekedwa. Ife tingoyenera kukhulupirira Yesu kukhala mpulumutsi ndi ambuye ndipo tipulumutsidwa.  Genesis 11:10-32, all the generations starting with Adam, Seth, Noah, Shem and Abram who later became Abraham, all are leading us to Jesus Christ who is the salvation of all people. All of us today are blessed because we're in the time where all the signs leading us to Jesus came to an end and the salvation was given. All we need to do is to believe that Jesus is our lord and saviour and we are going to be saved.
Nov 21, 202251:34
Kodi umodzi ndi mphamvu?Is oneness a sign of power?

Kodi umodzi ndi mphamvu?Is oneness a sign of power?

Genesis 11:1-9, nthawi zambiri timakamba zokhuza umodzi mokondwera mkumati umodzi ndi mphamvu. Kodi ndi chonchodi? Eya, mokuti Baibulo limalimbikitsa umodzi kufikira pakuti Yesu anati, pali awiri nanenso ndimakhala pomwepo. Koma umodzi omwe ulinga wa Nimurodi, ziwani kuti mulungu amadana nawo ndipo amatsika kuzadzetsa kusamvana pakati pa onse ozondosa zabwino kusandusa zoipa. Genesis 11:1-9, most of the times we speak of oneness with joy saying, in oneness there is power. But is that true? Yes it is, the Bible encourages oneness to the point that Jesus said, where they're two people am also there. But the oneness that mimic Nimrod, better know that God hates that and he comes down and cause confusion amongst those who exchanges goodness for badness. 
Nov 09, 202201:12:31
Mulungu amakwaniritsa malonjezano ake/God fulfils his promises

Mulungu amakwaniritsa malonjezano ake/God fulfils his promises

Genesis 10:1-32, mu chaputara chimenechi tikuona ndandanda wa ana a Nowa. Koma nkhani yayikulu yagona pa Semu. Kuchokera kwa Semu kunabadwa mwana yemwe anabereka mwana yemwe anaberekanso mwana yemwe anali tate wa Abrahamu komwe mbewu ya mzimayi ikudzera kufikira pa Yesu Khristu. Mulungu atalonjeza kwa mzimayi uja mumachaputara oyambirira aja za mbewu yomwe izaphwanya mutu wanjoka mubukuli, tikuona kuti akusunga pangano lake pomwe akusunga mbewu imeneyi kudzera mwa Semu. Mulungu amakwaniritsa malonjezano ake. Genesis 10:1-32, in this chapter we are getting the full detailed genealogy of the sons of Noah and their descendants. But the main story focuses on Shem. It is from Shem where a son was born who gave birth to a son who later on became the father of Abraham through whom the seed of a woman continued until Jesus Christ. After God promised the seed of a woman in the early chapters of this book, God preserves that seed through Shem until Abraham and so on and so forth. God fulfils his promises.
Nov 01, 202241:19
Kugonjetsa Zoipa Pakuchita Zabwino/Defeating Evil by Doing Good

Kugonjetsa Zoipa Pakuchita Zabwino/Defeating Evil by Doing Good

Genesis 9:18-28, Nowa atatuluka mchombo anayamba kulima nthaka monga momwe Adamu ankachitira. Nowa anali munthu woyambilira kulima mphesa. Munkhaniyonse tikuona kuti kumapeto kwake kwa kulima mphesaku kukubweretsa mavuto omwe anatsatiridwa ndi themberero. Tikuonanso kuti ana aamuna a Nowa ndikomwe kunachokera mitundu yonse ya anthu pa dziko lapansi. Zimene nkhaniyi ikutanthauza ndi izi: nthawi zonse makolo amakhala ndi udindo wawukulu ophunzitsa anawo njira zoti ayendemo ndipo anawo zomwe aphunzitsidwa ndi zomwezo azakhale kutsogolo. Nde nchifukwa chake makolo ngati saphunzitsa ana awo makhalidwe abwino, anawo azalangidwa. Komanso sibwino kumafunira ena zoipa, m'malo mwake kumawapempherera popeza tonsefe ndife amodzi mwa khristu yesu. Genesis 9:18-28, After Noah came out of the ark, he started cultivating the land just like Adam did. Noah was the first to cultivate the vine yard. Then the whole story tells us that the cultivating of the vine yard ends with problems followed by a curse. We also see that the world's population came from the three sons of Noah. What the story means: all the time parents have the big responsibility of teaching their children the right way they should go. And whatever the children are taught, that will be conducted through out their whole lives. Then that's why, if parents do not teach their children the righteous way and they are wicked they will nee punished. And also, its not good to wish ill upon others, instead pray for them/each other for we are one in christ Jesus.   
Oct 27, 202201:02:13
Pangano La Mulungu Ndi Nowa/The Covenant Of God With Noah

Pangano La Mulungu Ndi Nowa/The Covenant Of God With Noah

Genesis 9:8-17, Mulungu atakondweretsedwa ndi Nowa chifukwa cha kumvera kwake, anamudalitsa namuuza kuti "abelekane ndipo adzadze dziko lapansi ndikuligonjetsa." kenaka Mulungu anachita naye pangano Nowa namuuza kuti sazawononganso dziko lapansi ndi madzi. Izi zinali zosangalasa kwa Nowa ndi banja lake. Komatu izi sizikutanthauza kuti Mulungu sazalanganso dziko lapansi chifukwa cha machimo a anthu. Ayi konse, zowona zake n'zakuti, kuli chilango china chomwe chasungilidwa anthu ochimwa chomwe ndi chowopsa kuposa chanthawi ya Nowa. Genesis 9:8-17, After God was pleased with Noah because of his obedience, he blessed him and told him to "be fruitful and become many and subdue the earth." Then God went on and made a covenant with Noah. He said 'never again will I destroy the earth with flooding waters.' This was good news for Noah and his family. But does that mean that God will never destroy wicked people? Not at all, in fact the bible says that there is a greater judgement restored for those who are wicked and disobedient to God and it is severe than that of Noah.  
Oct 20, 202244:22
Noah received a blessing through obedience to God/Nowa analandira M'dalitso kudzera mukumvera Mulungu

Noah received a blessing through obedience to God/Nowa analandira M'dalitso kudzera mukumvera Mulungu

Genesis 9:1-7, Noah did everything that God asked of him, he never questioned God or refuse his commandments. But followed God's instructions through out his entire life even when building the Ark, he kept on following God's own directions. And because of this, God was impressed with Noah, so he blessed him and told him that "be fruitful and multiply, fill the earth and subdue it." This is like wise to us christians today, if we obey God's word and follow his instructions, it is to no doubt that he will bless us like he did Noah. Genesis 9:1-7, Nowa anachita zonse zomwe Mulungu anamulamulira, iye sanafunse konse zochita za Mulungu kapena kukana malaturo ake. Koma anatsatira malangizo a Mulungu moyo wake wonse ingakhale pomanga chombo, anapitilira kutsatirarabe malangizo ake. Ndipo chifukwa cha ichi, Mulungu anakondwera naye Nowa namudalitsa kuti mubelekane ndi kuchulukana ndi kuligonjetsa dziko la pansi. Izi zili chimozimozi ifenso a khristu lero, ngati timvera mulungu ndi mawu ake, popanda kukayikira Mulungu adzatidalitsa nafenso monga momwe anachitira Nowa. 
Oct 11, 202256:31
Spiritual Warfare/Nkhondo ya uzimu

Spiritual Warfare/Nkhondo ya uzimu

Revelation chapter 8, Dr Eric continues exploring the book of revelation. The book of revelation, for proper understanding of the book, two things to consider; 1) the use of metaphoric language. this is important to take note of, because it would be very difficult to take everything you hear in the book to be literal. for example, when the book talks about the beast of ten horns and the face of a lion, that is metaphoric it's not literal. 2) the book of revelation is written in a loop, meaning to say its sayings and meanings are constructed in a way that is considered to be known as a loop not linear structuring, thus if you happen to read the book as you would any other books, having the beginning, body then the end, you would miss out everything. In this chapter, we hear of the seven trumpets. These are the judgements God is pouring out on the earth. The judgements goes along, chapters 9, 10, 11 up to 13. And the of exodus helps us to understand more of these judgements by shading the picture of how they are to take place. In chapter 7 of exodus, God frees his people with his majestic hand by using the ten plagues. The same, God will do to free his people once and for all with his hand by the means of the judgements also known as the seven trumpets. Chivumbulutso 8, Dr Eric akupitiliza kuwunikira zomwe zikuchitika mu buku la chivumbuliutso. Buku la chivumbulutso, kuti munthu ukhale ndi kumvetsesa koyenerera kwa bukuli, njira ziwiri zikuyenera kusatidwa. 1) kagwiritsidwe ntchito ka mizembayiso. bukuli likamakamba za Chilombo cha nyá'nga khumi limodzi ndi khope ya nkango, ndizembayiso umenewo. Kuzilingalira malinga ndi mmowe zikumvekera ndekuti uthenga onse usokonezeka kamvekedwe kake. 2) buku la chivumbulutso linalembedwa mozungulira, mokuti munthu ngati angawerenge bukuli monga achitira mabuku ena omwe amakhala ndi chiyambi kenaka thunthu kumaliza ndi chimaliziro ndekuti uthenga onse waphonyedwa. Mu chaputara cha 8, tkuwuzidwa za malipenga asanu ndi awiri, omwe akuyimirira chiweruzo cha mulungu pa dziko lapansi. Chiweruzochi chikuyenda mu machaputara awa 9, 10, 11 mpaka 13. Komanso buku la exodo 7, limathandiziranso kumvetsesa kowonjezera makamaka momwe chiweruzo chomwe chili mbuku la chivumbulutso chikuchitikira.
Oct 06, 202201:12:58
Kodi muli mbali iti m'masiku omalizawa?/What side are you on in these ladder days?

Kodi muli mbali iti m'masiku omalizawa?/What side are you on in these ladder days?

Chivumbulutso chaputara 7, mu chaputara chimenechi Dr. Eric akupitiliza kubweletsa poyera za nsautso waukulu m'masiku omaliza. Kamvetsetsedwe ka nthawiyi kakupitilirabe kukhala kovutirapo kwa anthu ena kamba kuti kalembedwe kozembayisa kakupitilirabe kupezeka ingakhale mu chaputarachi. Panthawi yomweyo tikuona kuti Paulo akulemba chaputarachi mundondomeko yomwe ingafananizilidwe ndi mapiri omwe patali akuoneka ngati Phiri limodzi koma pomwe uwandikira ndipomwe ungazindikire kuti ndi mapiri omwe akupezeka mondondozana. Zinthu zochitika m'masiku omalizawa zikupezeka zomwe zikutchulidwa kuti zimatiro zisanu ndi ziwiri zomwenso kalembedwe kake ndi kozembayisa. Munthawi imeneyi ndichanzeru kuzifunsa kuti kodi tili mbali iti? popeza nthawi nde yatha kale. Revelation chapter 7, in this chapter Dr. Eric continues to explore the great tribulation in the ladder days. The understanding of the ladder days and the great tribulation continues to be hard to others as the chapter continues to have the writings that uses the metaphoric language. And at the very time, we see that Paul is writing the chapter in a loop which also can be liken to mountains, from afar, they look like one big mountain but as you get closer and closer, you begin to see that they are but many mountains as you move along them. The great tribulation is also told in the way that the seven scrolls unfolds. At this point it is right to ask the question what side are you on? as we see the days drawing near to the end. 
Sep 21, 202230:26
Kupembedza Koona ndi Kuvomereza ndi Mathokozo Chipulumutso cha Mulungu pa anthu ake/A proper worship is a proper response to God's salvation.

Kupembedza Koona ndi Kuvomereza ndi Mathokozo Chipulumutso cha Mulungu pa anthu ake/A proper worship is a proper response to God's salvation.

Genesis 8:15-22, Nowa akutiwonesera mtima omvera. Nowa anadikira mçhombo ngakhale anali akudziwa kuti madzi adali atawuma ndipo akadatha kutuluka, koma iye anadikira lamuro lochokera kwa Mulungu lomuuza kuti atha kutuluka limodzi ndi ziyama zonse zinali ndi iye mçhombomo. Panthawi yomweyo tikuona kuti chinthu chomwe chikukambidwa mobwereza chokhuza kumvera kwa Nowa ndichakuti iye anachita zonse zomwe mulungu anamulamurira zomwenso ndi chıthünzithunzi cha moyo wa Mesiya. Nowa atatulaka m'çhombo anamanga guwa la nsembe napsereza nsembe ngati njira imodzi yothekozera Mulungu kuti wapulumutsa iye pamodzi ndi banja lake. Mulungu atamva kunukhira kwake kwa nsembeyo anakondwera. Ifenso ngati akhristu tikuyenera kuonetsera mathokozo ndi ulemu kwa Mulungu ngati njira imodzi yopembezera moona, namuthokoza chifukwa cha chipulumutso chomwe tilinacho kudzera mwa Khristu yesu. Nowa anamanga guwa napsereza nsembe pofuna kuthokoza mulungu kamba ka chipulumutso, nafenso anthu tiyeni tipeleke matupi athu ngati nsembe yopsereza kwa Mulungu ngati njira yothokozera mulungu kamba ka chipulumutso ndipo iye azakondwera nafe. Genesis 8:15-22, Noah shows us a heart of obedience. Noah waited in the ark even though he knew that the water had dried up, he waited for the command from God telling him to get out of the ark along with the animals with him. And as far as the obedience of Noah is concerned, we are told that he did everything that God commanded him to do and he did just so. After he had come out of the ark, he built an altar and offered up a sacrifice to God thanking him for the salvation. When God smelled the aroma of the sacrifice, he was pleased. As true christians we need to show gratefulness and respect to God as way of thanking him for the salvation we have in Christ Jesus. Noah built an altar and offer a sacrifice to God, while as we need to offer our bodies as a living sacrifice and he will be pleased with us.
Sep 19, 202258:52
Chivumbulutso cha nthawi ya "msautso" m'masiku omaliza/The Revelation of the "great tribulation" in the ladder days

Chivumbulutso cha nthawi ya "msautso" m'masiku omaliza/The Revelation of the "great tribulation" in the ladder days

Chivumbulutso 6:1-6, Abusa a Eric, akubweletsa poyera za msautso omwe ukuza pa dziko la pansi m'masiku omaliza. M'buku la chivumbulutso chaputara chachisanu ndi chimodzi, chikukamba za zimatiro zisanu ndi ziwiri zomwe kumvetsetsa kwake kumakhala kovutilapo chifukwa cha kagwilitsidwe ntchito ka mawu omwe ndi ozembayisa. Chifukwa chake anthu ambiri amakhala ndi mfundo zosiyanasiyana pa khani imeneyi. Kubweranso kwa Yesu Khristu kachikena kuzakhala ngati momwe koyamba kanalili. Ndipo ma vesi mu chaputarachi akukamba bwino lomwe za zomwe zikuyenera kuchitika m'masiku omaliza Yesu asanabwere.   Revelation 6:1-8, Pastor Eric, brings to light the great tribulation in the ladder days. The book of revelation chapter six, talks about the seven seals where by the language used is metaphoric which is very difficult to understand and this is also the reason why so many people have different views about this very subject. The second coming of Jesus Christ will much be like the first one. And the verses in this chapter explains very well the things to take place before the second coming of Jesus Christ.
Sep 15, 202250:22
Jesus the lord of History, the lord of the world

Jesus the lord of History, the lord of the world

Maliko 6:30-44, M'ma vesi amenewa tikuonetseredwa bwino lomwe za m'momwe mbiri m'baibulo ikuonetsera dongosolo lomwe Mulungu analikonza kale lokhuza kubwera kwa khristu pa dziko lapansi kuzapulumutsa anthu ake. Mwachitsanzo, aneneri angapo akutengeredwa ku malo, kapena akupita kumalo omwe kulibeko chakudya kapena chakudyacho ndichochepa. Aneneri monga Mose, Eliya ndi ena otero, pomwe izi zikuwachitikira akupelekera ulosi wa yesu khristu yemwe ndi tate wa mbiri ndi dziko. Muzochitika zonsezi zomwe aneneriwa akukumananazo mulungu akuchulukisa chakudya, kapena kupeleka chakudyacho. Yesu atabwera pa dziko lapansi anakwaniritsa ulosi umenewo pomwe anadyetsa anthu 5000 posawerengera azimayi ndi ana. Mbuye kapena tate wa mbiri yesu khristu, akudyetsa anthu ambiri kukwaniritsa zomwe mbiri yakhala kulosera za iye. Mark 6:30-44, In these verses we are seeing clearly how the history written in the bible is showing the plans God put in place along time ago  of sending his son to the earth to die and redeem his people. For example, prophets are often taken to places or are told to go to places where either the food is few or not at all. Prophets like Moses, Elijah and many others, as these things are happening to them, they're painting out the clear picture of the life of the christ who is the lord of history and of the world. So the lord is either multiplying the food or provides the food in the cases of the prophets. When Jesus came to the earth, he lived out those examples where by he multiplied the food and fed the thousands.  
Sep 05, 202254:57
Mulungu Avumbulutsa Chilungamo ndi Chisomo chake/God reveals his Justice and Grace

Mulungu Avumbulutsa Chilungamo ndi Chisomo chake/God reveals his Justice and Grace

Genesis 7:1-10, Mmavesi amenewa tikuphunzira za chenjezo lomwe lina pelekedwa munthawi ya Nowa pomwe anthu ankangodya, kumwa, kukwatira ndi kukwatiwa kufikira Nowa analowa mchombo ndipo chigumula chinabwera. Zomwe ndi chimodzimodzi munthawi yathu lero, pomwe anthu akungodya, kumwa, kukwatira ndi kukwatiwa. Panthawi yomweyo tikuona za kulungama kwa Nowa komwe kwabwera chifukwa chachikhulupiriro chake pa Mulungu, pomwe anachenjezedwa za chigumula iye anakonza chombo choti apulumutsire banja lake pamodzi naye. Ndipo muzonse Nowa anachita monga momwe Mulungu anamuwuzira. Genesis 7:1-10, In these verses, we're learning of the warning given in the days of Noah when the people were only eating, drinking, marrying and being given into marriage, until Noah entered the ark and the door was shut from behind and the flood came. This is the same with our time, people are only eating, drinking, marrying and being given into marriage. At the same time, we're learning of Noah's righteousness through faith. when he was given the divine warning, Noah constructed the ark to preserve the lives of his family including his. And in everything Noah did exactly as God commanded him to do.
Aug 03, 202241:56
Nowa ndi chigumula/Noah and the flood

Nowa ndi chigumula/Noah and the flood

Genesis 6:9-22, chiwawa chinadzadza pa dziko lapansi kotero kuti dziko linakhala lowonongeka pamaso pa Mulungu.Izi zinapangisa Mulungu kutsindikadi kwa Nowa kuti sachitiranso mwina koma kuliwononga dziko lapansi ndi zamoyo zonse. Koma Nowa anali munthu wolungama ndiwopanda tchimo pakati pa anthu a m'bado wake. Ndipo Nowa anayenda ndi Mulungu. Genesis 6:9-22, But the earth had become ruined in the sight of the true God, and the earth was filled with violence. God told Noah that he had decided to put an end to all flesh, because the earth is full of violence on account of them, so I am bringing them to ruin together with the earth. But Noah was a righteous man. He proved himself faultless among his contemporaries. Noah walked with the true God.   
Jul 26, 202254:18
Yehova akomera mtima Nowa/Jehovah favours Noah

Yehova akomera mtima Nowa/Jehovah favours Noah

Genesis 6:5-8, Kuyipa kwa munthu pa dziko la pansi kumakulirakulirabe ndikuti nthawi zonse amalingalira ndikukhumbira kuchita zoyipa zokhazokha, Yehova anamva chisoni kuti analenga munthu ndikumuyika pa dziko lapansi, ndipo anawawidwa mtima. Genesis 6:5-8, Consequently ,Jehovah saw that man's wickedness was great on the earth and that every inclination of the thoughts of his heart was only bad all the time. Jehovah  regretted that he had made men on the earth , and his heart was saddened.
Jul 19, 202220:53
Kuyipa kwakulu kwa anthu

Kuyipa kwakulu kwa anthu

Genesis 6:1-4, ikulongosola za chiyambi chachionongeko cha dziko la pansi ndi chilengedwe chonse chimene Mulungu anachilenga. Mulungu akuononga chilengedwe chonse chomwe anachilenga chifukwa chakuti chilengedwecho (Anthu) chamukana Mulungu. Genesis 6:1-4, these verses are basically focusing the discussion on the cause of the destruction of the world and its creation. God is rejected by his creation (Humans) thus humans wants to rule themselves instead of being ruled  by God.
Jul 11, 202201:00:25
Banja la Kaini ndi Mbewu ya mzimayi

Banja la Kaini ndi Mbewu ya mzimayi

Genesis 4:17-26, ikukamba za banja la Kaini komanso kubweresa poyera kupitirira kwa kusamvera kwa Kaini ndi mtundu wake wonse. Izi zili chomwecho pomwe tikuwona Lameki akukwatira akazi awiri motsutsana ndi dongosolo la ukwati lomwe Mulungu analikhadzikitsa kuti mwamuna akuyenera kukwatira mkazi m'modzi. Panthawi yomweyo tikuwonanso zokhuza mbewu ya mzimayi yomwe ikubwera kudzera mwa Seti yemwe akubadwa ku banja la Adamu ndipo Seti akulowa m'malo mwa Abele yemwe Kaini anamupha. Genesis 4:17-26, is discussing the family of Cain and continuing to bring to light the ungodly actions of Cain and his descendants when we see La'mech marrying two wives which is against God's marriage order which says that a man is to marry one wife. It is also discussing the seed of a woman where we see the birth of Seth to the family of Adam who is now replacing Abel who Cain killed. 
Jul 04, 202252:14
Mdalitso wochokera kwa Mulungu kupita kwa ana a Adamu ndi Zotsatira zake/Blessings from God upon Adam's children and their response.

Mdalitso wochokera kwa Mulungu kupita kwa ana a Adamu ndi Zotsatira zake/Blessings from God upon Adam's children and their response.

Mulungu akudalitsa Kaini komanso Abele panthawi yomwe agwira ntchito zawo ndipo iwo akulandira zotsatira zabwino kuchokera ku ntchito zawozi. Panthawi yomweyo tikuona kuthokoza kosiyana komwe kukubwera kuchokera kwa anthu awiriwa omwe agwira ntchito zosiyana pomwe apeleka nsembe zawo kwa Mulungu. God blesses Cain and Abel when doing their separate work and are blessed abundantly while on the other Hand we see how they both thank God by offering up sacrifices but with different attitudes. 
Jun 21, 202201:10:59
Chilungamo ndi Chisomo Adam ndi Hava atachimwa |Justice and Grace after the fall

Chilungamo ndi Chisomo Adam ndi Hava atachimwa |Justice and Grace after the fall

Genesis 3:17-24, mu uthenga uwu tikuona chilungamo cha mulungu chikuonetsedwa chifukwa cha kusamvera kwa Adamu, komanso tikuona mulungu akupeleka chisomo kwa Adamu chifukwa cha chikhulupiriro chake. Chilungamo cha mulungu chinaonekera mu chilango chomwe chinapelekedwa kwa Adamu chifukwa cha tchimo lake. M'dzanja linali tikuona mulungu akuonetsa chisomo kwa Adamu pamene anakhulupirira malonjedzo a mulungu. Genesis 3:17-24, in this Sermon we see both God's justice and his grace displayed in response to man's disobedience and faith respectively. God's justice is served as judgement is passed on to Adam after his disobedience while on the other hand God responds to Adam's faith with grace when he shade the blood of an innocent animal to cover their shame which is a shadow of the sacrificial death of Christ.
Jun 13, 202248:23
Chulukitsani Alimi | Multiply Farmers

Chulukitsani Alimi | Multiply Farmers

Pamene tapanga ophunzira, tiziyembekezera ophunzira atsopano kupanganganso ophunzira ochuluka. Pamene tawazindikira, tikuyenera kuwaphunzitsa komanso kuwatumiza ophunzira atsopanowa. Tikatero timakhala kuti tatumiza alimi ochulukira m’minda ku ntchito yodzala mipingo. When we make disciples, we should expect new disciples to make more disciples. When we identify, invest in, and send out these new disciples, we send more farmers into other fields for the work of church planting.
Dec 02, 202021:19
Kololani m’Munda | Harvest the Field

Kololani m’Munda | Harvest the Field

Pamene talalikira uthenga wabwino ndikuphunzitsa okhulupirira atsopano, ndi nthawi yoti tiwakhonzekeretse okhulupirira atsopano kuti akhale mpingo. Mpingo umakhala ndi anthu omwe ndi ziwalo ndipo amasonkhana pamodzi kuti amve ulaliki wa baibulo. Mpingowo umachita ubatizo ndi mgonero wa ambuye ndipo umatsogozedwa ndi abusa ndi atumiki. After we have preached the gospel and discipled new believers, it is time to organize the new believers into a church. A church consists of member that assemble together for biblical preaching. It practices baptism and the Lord’s Supper and is led by pastors and deacons.
Dec 02, 202029:53
Samalirani m’Munda | Tend the Field

Samalirani m’Munda | Tend the Field

Monga munda omwe wayamba kukula, akhirisitu atsopano amafunika chisamaliro chauzimu pafupipafupi. Yesu akutilamula kuti tibatize wokhulupirira atsopano ndi kuwaphunzitsa malamulo ake. Like a field that has started to grow, new Christians need constant spiritual care. Jesus commands us to baptize new believers and to teach them his commands.
Dec 02, 202022:23
Dzalani m'Munda | Sow the Field

Dzalani m'Munda | Sow the Field

Kudzala kachisi wa tsopano kuchokera mubaibulo, tikuyenera kudzala munda ndi mbewu ya uthenga wa wabwino. Izi zimafunika kuti tifalitse uthenga wa bwino momveka bwino komanso kwa anthu ambiri. Pamene tifalitsa uthenga wa mulungu, Yesu akutiuza kuti tiyembekeze mayankho anayi (Marko 4:11-20). To biblically plant a new church, we must sow the field with the seed of the gospel. This requires us to proclaim the gospel clearly and widely. When we proclaim the gospel, Jesus tells us to expect four different responses (Mark 4:11–20).
Dec 02, 202019:47
Limani m'Munda | Prepare the Field

Limani m'Munda | Prepare the Field

Timakhonza munda watsopano wodzalapo mpingo kudzera mupemphero. Timamupempha Mulungu kuti akonzekeretse nthaka yoti ilandire mbewu ya uthenga wa bwino. Koma tikuyeneranso kuzikonzekeretsa tokha popanga kafukufuku wa munda, kufunafuna munthu wamtendere, ndi kupanga ndondomeko zokaphunzitsa uthenga wabwino. We prepare a new field for church planting through prayer. We ask God to prepare the soil to receive the seed of the gospel. But we must also prepare ourselves by researching the field, seeking a person of peace, and making plans to preach the gospel.
Dec 02, 202027:10
Minda Inayi | The Four Fields

Minda Inayi | The Four Fields

Cholinga chathu ndikupanga ophunzira ndipo timapanga ophunzira polalikira uthenga wabwino ndi kudzala mipingo. Kuti tidzale mpingo timayenera kukonza munda, kudzala mmunda, kusamalira munda kenaka kukolola mmunda. Our goal is to make disciples, and we make disciples by sharing the gospel and planting churches. To plant churches, we must prepare the field, sow the field, tend the field, and then harvest the field.
Dec 02, 202021:06
Pirirani Mpaka Kumapeto | Endure to the End

Pirirani Mpaka Kumapeto | Endure to the End

Akolose 3:4; Yakobo 1:2-4. Imfa ya Yesu siikutitsimikizira kupindula. Akhirisitu amavutika. Koma kuvutika kumeneku ndi kuyesedwa kwa chikhulupiliro chawo.  Iwo amene amakhulupiliradi sangataye chiphulumutso chawo konse, komano chikhulupiliro choonadi chimazindikirika pamene akhalabe okhulipirika mpaka kumapeto. Colossians 3:4; James 1:2–4. Jesus’ death does not guarantee us prosperity. Christians suffer, but this suffering is a test of our faith. Those who truly believe can never lose their salvation, but true faith is demonstrated only by remaining faithful to the end.
Dec 02, 202028:46
Vulani Chikhalidwe cha Uchimo | Take Off Sin

Vulani Chikhalidwe cha Uchimo | Take Off Sin

Akolose 3:5-10; 1Yohane 1:5-9; Marko 7:21-23; Yakobo 1:14-15. Ana a Mulungu si a ngwiro. Amatha nthawi zina kuchimwa koma ana a Mulungu amavomereza matchimo awo ndipo amafunafuna kupha machimo awo kuchokera ku mizu po khonzanso malingaliro awo ndikuvala munthu watsopano. Colossians 3:5–10; 1 John 1:5–9; Mark 7:21–23; James 1:14–15. Children of God are not perfect. They do sometimes sin. But Children of God confess their sins and seek to kill their sin at the root by renewing their minds and putting on the new self.
Dec 02, 202026:29
Kutsindikizidwa ndi Mzimu Woyera

Kutsindikizidwa ndi Mzimu Woyera

Mulungu watitsindikiza ndi Mzimu Woyera kutitsimizira kuti chipulumutso chathu ndi chamuyaya. Komanso kuti madalitso onse achipulumutso athu tizalandi kutsogolo.
Aug 05, 202036:59
Kupembeza Limodzi ndi Banja | Worship with Family

Kupembeza Limodzi ndi Banja | Worship with Family

Akolose 3:18–21; Yoswa 24:15; Deuteronomo 6:6–9. Pamene Mulungu anakupangani kukhala atsopano, anayamba kupanga banja lanu kukhanso latsopano. Pangani Mulungu ku khala Mulungu wa banja lanu kudzera mukupembeza kwa banja. Colossians 3:18–21; Joshua 24:15; Deuteronomy 6:6–9. When God made you new, he began to make your family new. Make God the God of your home through family worship.
Aug 05, 202024:24
Kondani Anthu Ena | Love Others

Kondani Anthu Ena | Love Others

Akolose 3:12–13; Yohane 13:34–35. Dziko lidzadziwa kuti ndife ana aMulungu kudzera mu chikondi chathu. Baibulo likutilamulira ife kuti tikonde Mulungu, anasi utuu, wina ndi m'dzake, adani athu, komanso iwu omwe ndi osowa. Colossians 3:12–13; John 13:34–35. The world will know we are children of God by our love. The Bible commands us to love God, neighbor, one another, enemies, and those in need.
Aug 05, 202027:52
Kuchita Umboni wa Yesu | Witness about Jesus

Kuchita Umboni wa Yesu | Witness about Jesus

Akolose 3:1–4; 4:5–6; Machitidwe 1:8. Mulungu akuyitana mKhristu wina aliyense kukhala mboni ya Yesu. Kuchitira umboni wokhudzana ndi Yesu ndi kosavunga monga kuyakhula nkhani yako ndi nkhani ya Mulungu. Colossians 3:1–4; 4:5–6; Acts 1:8. God calls every Christian to be a witness about Jesus. Witnessing about Jesus is as easy as telling your story and telling God's story. Preacher: Dr. Joshua Hutchens Class: Kukhala Wophunzira: Kukhala Moyo Wosinthika ndi Uthenga Wabwino | Discipleship: Living the Gospel Translator: Isaac Dzimbiri
May 27, 202023:08
Perekani ku Mpingo Wanu | Give to Your Church

Perekani ku Mpingo Wanu | Give to Your Church

Machitidwe 2:45; 2 Akorinto 9. Timapereka chifukwa Mulungu anatipatsa ife Mwana wake. Tikuyenera kukhala ndi dogosolo la kupereka kwathu komanso tikuyenera kupeka wokondwera. Acts 2:45; 2 Corinthians 9. We give because God gave us his Son. We need to plan our giving and to give cheerfully. Preacher: Dr. Joshua Hutchens Class: Kukhala Wophunzira: Kukhala Moyo Wosinthika ndi Uthenga Wabwino | Discipleship: Living the Gospel Translator: Isaac Dzimbiri
May 24, 202021:07
Imfa, Chiwukitso komanso Mapemphero a Yesu Khristu Tsopanolingo

Imfa, Chiwukitso komanso Mapemphero a Yesu Khristu Tsopanolingo

Oyera mtima apirira muchikhulupiriro chawo chifukwa imfa ya Yesu yachotsa chostutsa china chilichonse komanso mlandu uliwonse otsutsana ndi sosakhidwa a Mulungu. Chiukitso cha Yesu ndi chitsimikizo cha chikhulupiriro chathu komanso mpemphero ake opemperera oyera mtima amatsimikizira kuti chikhulupiriro cho sichifowoka. Preacher: Isaac Dzimbiri Class: Kudzama Choonadi Series: Kupirira kwa Oyera Mtima Chikhulupiriro Chawo
May 21, 202001:14:50
Sonkhani Pamodzi kuti Mupembeze | Gather for Worship

Sonkhani Pamodzi kuti Mupembeze | Gather for Worship

Machitidwe 2:42; Ahebri 10:24–25. Timasokhana pamodzi kuti tipembeze ndi cholinga choti tithandizone wina ndi nzake kukula musinkhu mwa Khristu. Tikuyenera kukhala ndi chikhalidwe chopembera ndi mpingo umodzi nthawi zonse. Acts 2:42; Hebrews 10:24–25. We gather to worship to help one another grow to maturity in Christ. We must make worship with our church a habit. Preacher: Dr. Joshua Hutchens Class: Kukhala Wophunzira: Kukhala Moyo Wosinthika ndi Uthenga Wabwino | Discipleship: Living the Gospel Translator: Isaac Dzimbiri
May 19, 202030:37
Werenga Baibulo | Read the Bible

Werenga Baibulo | Read the Bible

Machitidwe 2:42; 2 Timoteyo 3:16–17. Kudzera mukuwerenga Baibulo, timamva Mulungu akuyakhula nafe. Khalani ndi dogosolo lakawerenge ka Baibulo komanso yambani kuwerenga. Konzekerani Kuwerenga Baibulo: https://chiphunzitsochoona.com/wp-content/uploads/2020/05/Bible-Reading-Plan-Chichewa.pdf Acts 2:42; 2 Timothy 3:16-17. By reading the Bible, we hear God speak to us. Have a plan for reading the Bible, and get started. Bible Reading Plan: https://chiphunzitsochoona.com/wp-content/uploads/2020/05/Bible-Reading-Plan-English.pdf Preacher: Dr. Joshua Hutchens Class: Kukhala Wophunzira: Kukhala Moyo Wosinthika ndi Uthenga Wabwino | Discipleship: Living the Gospel Translator: Isaac Dzimbiri
May 16, 202030:20
Yambani Kupemphera | Start Praying

Yambani Kupemphera | Start Praying

Kudzera mupemphero, timamva umwana wathu mubanja la Mulungu. Yesu anatiphuzitsa momwe tikuyenerera kupemphera munjira yomwe ikuyenerera ku pereka ulemerero kwa Mulungu. Through prayer, we experience our adoption into God's family. Jesus taught us how to pray in a way that glorifies God. Preacher: Dr. Joshua Hutchens Class: Kukhala Wophunzira: Kukhala Moyo Wosinthika ndi Uthenga Wabwino | Discipleship: Living the Gospel Translator: Isaac Dzimbiri
May 11, 202043:34
Mphamvu za Mulungu Zosunga Oyera Mtima

Mphamvu za Mulungu Zosunga Oyera Mtima

Chifukwa cha mphamvu za Mulungu ndi chifuniro chake, anthu woyera mtima apirira mu chikulupirira chawo mpaka kumapeto kwa moyo. Preacher: Isaac Dzimbiri Class: Kudzama Choonadi Series: Kupirira kwa Oyera Mtima Chikhulupiriro Chawo
May 07, 202049:38
Batizidwani | Be Baptized

Batizidwani | Be Baptized

Ubatizo ndi njira yoyambirira ya kumvera monga mKhristu watsopano. Uma onetsera kwa aliyense yemwe alikunja zomwe Mulungu wachita kuti mwa munthu. Baptism is your first step of obedience as a new Christian. It is the public sign of your faith. It shows to everyone outside what God has done inside. Preacher: Dr. Joshua Hutchens Class: Kukhala Wophunzira: Kukhala Moyo Wosinthika ndi Uthenga Wabwino | Discipleship: Living the Gospel Translator: Isaac Dzimbiri
May 05, 202026:30
Uthenga Wabwino ndi Mphamvu ya Mulungu | The Gospel is the Power of God

Uthenga Wabwino ndi Mphamvu ya Mulungu | The Gospel is the Power of God

Aroma 1:16–17. Uthenga Wabwino ndi mphamvu ya Mulungu yopulumutsa chifukwa mu Uthenga Wabwino mphatso ya Mulungu ya chilungamo ya onetsedwa. Romans 1:16–17. The gospel is the power of God for salvation because in the gospel God's gift of righteousness is revealed. Preacher: Dr. Joshua Hutchens Class: Kuyenda m'Choonadi | Walking in Truth Series: Aroma | Romans Translator: Isaac Dzimbiri
May 03, 202031:46
Kodi ndi chifukwa chiyani ukuyenera kudziwa kuti ndiwe wochimwa usanapulumutsidwe?

Kodi ndi chifukwa chiyani ukuyenera kudziwa kuti ndiwe wochimwa usanapulumutsidwe?

Funsa Mafunso: Kodi ndi chifukwa chiyani ukuyenera kudziwa kuti ndiwe wochimwa usanapulumutsidwe? Ask a Question: Why must you know you are a sinner before you can be saved? Preacher: Dr. Joshua Hutchens Translator: Isaac Dzimbiri
May 02, 202019:17
Chikondi cha Mulungu Chitsimikiza Kupirira kwa Oyera Mtima m'Chikhulupiriro

Chikondi cha Mulungu Chitsimikiza Kupirira kwa Oyera Mtima m'Chikhulupiriro

2 Timoteyo 1:9. Kupirira kwa anthu wokhulupirira kwa khazikika mu chikondi chosatha cha Mulungu, yemwe anatipatiratu chisomo chake mwa Yesu Khristu kutiwombola ife ku machimo athu. Preacher: Isaac Dzimbiri Class: Kudzama Choonadi Series: Kupirira kwa Oyera Mtima Chikhulupiriro Chawo
Apr 30, 202041:05
Timagwira ntchito chifukwa Mulungu akugwira ntchito | We work because God works

Timagwira ntchito chifukwa Mulungu akugwira ntchito | We work because God works

Mulungu wakulenga iwe kukhala watsopano. Tsono timamvera Mulungu chifukwa timamukonda Mulunguyo, ndipo timamumvera, Mulungu amagwira ntchito mwaife. God has made you new. So we obey God because we love God, and as we obey, God works in us. Preacher: Dr. Joshua Hutchens Class: Kukhala Wophunzira: Kukhala Moyo Wosinthika ndi Uthenga Wabwino | Discipleship: Living the Gospel Translator: Isaac Dzimbiri Episode Page: https://chiphunzitsochoona.com/sermon/1-timagwira-ntchito-chifukwa-mulungu-akugwira-ntchito
Apr 28, 202026:15
Mulungu wagonjetsa kudzera mwa Mwana wake | God has conquered through his Son

Mulungu wagonjetsa kudzera mwa Mwana wake | God has conquered through his Son

Aroma 1:8–15. Chigonjetso cha Mwana wa Mulungu chitha kuonekera mu chikhulupiriro chathu komanso mukulalikira Uthenga Wabwino ku mayiko onse. Romans 1:8–15. The victory of God's Son can be seen in our faith and in the preaching of the gospel to every nation. Preacher: Dr. Joshua Hutchens Class: Kuyenda m'Choonadi | Walking in Truth Series: Aroma | Romans Translator: Isaac Dzimbiri Episode Page: https://chiphunzitsochoona.com/sermon/mulungu-wagonjetsa-kudzera-mwa-mwana-wake
Apr 26, 202031:01
Dongosola la Mulungu pa Chipulumutso cha Oyera Mtima

Dongosola la Mulungu pa Chipulumutso cha Oyera Mtima

Aefeso 1:4–7; Aroma 8:29–30. Chipulumutso ya oyera mtima china yamba ndi Mulungu, ndipo chidzamulizidwa ndi Mulungu. Chifukwa choti Mulungu amatsiriza ndogosolo lomwe wa liyamba adzatsirizanso dogosolo la chipulumutso cha oyera mtima. Preacher: Isaac Dzimbiri Class: Kudzama Choonadi Series: Kupirira kwa Oyera Mtima Chikhulupiriro Chawo Episode Page: https://chiphunzitsochoona.com/sermon/dongosola-la-mulungu-pa-chipulumutso-cha-oyera-mtima
Apr 23, 202029:39
Mwapatulidwa ku Uthenga Wabwino | You are set apart for the gospel

Mwapatulidwa ku Uthenga Wabwino | You are set apart for the gospel

Aroma 1:1–7. Mulungu adatipatulidwa ife kuti tikalalikire Uthenga Wabwino ku mitundu yonse kwa ulemerero wa dzina la Mulungu. Romans 1:1–7. God set us apart to preach the gospel of Jesus Christ to all nations for the glory of God’s name. Preacher: Dr. Joshua Hutchens Class: Kuyenda m'Choonadi | Walking in Truth Series: Aroma | Romans Translator: Isaac Dzimbiri Episode Page: https://chiphunzitsochoona.com/sermon/mwapatulidwa-ku-uthenga-wabwino
Apr 22, 202036:39
Vomereza ndi Kukhulupirira | Confess and Believe

Vomereza ndi Kukhulupirira | Confess and Believe

Part 4 of 4 in Mphamvu za Mulungu Zopulumutsa | The Power of God for Salvation
Apr 19, 202021:14
Yesu ndi Mpulumutsi wanu | Jesus is your Savior

Yesu ndi Mpulumutsi wanu | Jesus is your Savior

Part 3 of 4 in Mphamvu za Mulungu Zopulumutsa | The Power of God for Salvation
Apr 12, 202015:07
Iwe ndiwe wochimwa | You are a sinner

Iwe ndiwe wochimwa | You are a sinner

Part 2 of 4 in Mphamvu za Mulungu Zopulumutsa | The Power of God for Salvation
Mar 29, 202020:12
Mulungu ndi wabwino | God is good

Mulungu ndi wabwino | God is good

Part 1 of 4 in Mphamvu za Mulungu Zopulumutsa | The Power of God for Salvation
Mar 22, 202015:28